Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 7:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Nyamukani mutakwiya, inu Yehova.

      Imirirani ndi kukhaulitsa adani anga amene andikwiyira.+

      Dzukani nʼkundithandiza, ndipo mulamule kuti chilungamo chichitike.+

  • Salimo 78:65, 66
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 65 Kenako Yehova anadzuka ngati kuti anali mtulo,+

      Ngati mmene amadzukira munthu wamphamvu+ pambuyo pomwa vinyo wambiri.

      66 Iye anathamangitsa adani ake nʼkuwabweza,+

      Anachititsa kuti adaniwo akhale onyozeka mpaka kalekale.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena