-
Oweruza 8:12Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
12 Zeba ndi Zalimuna atayamba kuthawa, iye anawathamangitsa mpaka kuwagwira. Mafumu a Midiyaniwa atagwidwa, gulu lawo lonse linachita mantha.
-