Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 96:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Lengezani pakati pa anthu a mitundu ina kuti: “Yehova wakhala Mfumu.+

      Dziko lapansi lakhazikika moti silingasunthidwe.*

      Iye adzaweruza mitundu ya anthu mwachilungamo.”*+

  • Chivumbulutso 11:16, 17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Ndipo akulu 24+ amene anali atakhala pamipando yawo yachifumu pamaso pa Mulungu aja, anagwada nʼkuwerama mpaka nkhope zawo pansi ndipo analambira Mulungu. 17 Iwo ankanena kuti: “Tikukuthokozani inu Yehova,* Mulungu Wamphamvuyonse, inu amene mulipo+ ndi amene munalipo, chifukwa mwatenga mphamvu zanu zazikulu nʼkuyamba kulamulira monga mfumu.+

  • Chivumbulutso 19:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Kenako ndinamva mawu amene ankamveka ngati mawu a khamu lalikulu, ngati mkokomo wa madzi ambiri komanso ngati mabingu amphamvu. Mawuwo anali akuti: “Tamandani Ya!*+ chifukwa Yehova* Mulungu wathu, Wamphamvuyonse,+ wayamba kulamulira monga mfumu!+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena