Salimo 34:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Siyani kuchita zinthu zoipa ndipo muzichita zabwino.+Yesetsani kukhala mwamtendere ndi ena komanso kuulimbikitsa.+ Salimo 101:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Sindidzayangʼana chinthu chilichonse choipa.* Ndimadana ndi zochita za anthu amene asiya kuchita zinthu zabwino.+Sindidzalola kuti zochita zawozo zindikhudze. Salimo 119:104 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 104 Ndimachita zinthu mozindikira chifukwa cha malamulo anu.+ Nʼchifukwa chake ndimadana ndi njira iliyonse yachinyengo.+ Aroma 12:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Chikondi chanu chisakhale chachiphamaso.+ Muzinyansidwa ndi zoipa+ nʼkumayesetsa kuchita zabwino. Aheberi 1:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Unkakonda chilungamo ndipo unkadana ndi kusamvera malamulo. Nʼchifukwa chake Mulungu, Mulungu wako, anakudzoza+ ndi mafuta achisangalalo chachikulu kuposa mafumu anzako.”+
14 Siyani kuchita zinthu zoipa ndipo muzichita zabwino.+Yesetsani kukhala mwamtendere ndi ena komanso kuulimbikitsa.+
3 Sindidzayangʼana chinthu chilichonse choipa.* Ndimadana ndi zochita za anthu amene asiya kuchita zinthu zabwino.+Sindidzalola kuti zochita zawozo zindikhudze.
104 Ndimachita zinthu mozindikira chifukwa cha malamulo anu.+ Nʼchifukwa chake ndimadana ndi njira iliyonse yachinyengo.+
9 Unkakonda chilungamo ndipo unkadana ndi kusamvera malamulo. Nʼchifukwa chake Mulungu, Mulungu wako, anakudzoza+ ndi mafuta achisangalalo chachikulu kuposa mafumu anzako.”+