Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Danieli 3:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Kenako Nebukadinezara ananena kuti: “Atamandike Mulungu wa Shadireki, Misheki ndi Abedinego+ amene anatumiza mngelo wake nʼkudzapulumutsa atumiki ake. Atumiki akewo anamudalira ndipo sanamvere lamulo la mfumu, moti anali okonzeka kufa* mʼmalo motumikira kapena kulambira mulungu wina aliyense kupatulapo Mulungu wawo.+

  • Mateyu 6:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Tithandizeni kuti tisagonje tikamayesedwa,*+ koma mutiteteze kwa woipayo.’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena