Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 31:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Adani anga onse amandinyoza,+

      Makamaka anthu oyandikana nawo.

      Ndipo anthu ondidziwa amachita nane mantha.

      Akandiona ndili panja amandithawa.+

  • Salimo 74:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Inu Mulungu, kodi mdani adzapitiriza kunyoza mpaka liti?+

      Kodi mdani adzachitira mwano dzina lanu mpaka kalekale?+

  • Salimo 79:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Anthu oyandikana nafe akutinyoza,+

      Anthu otizungulira akutiseka komanso kutikuwiza.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena