Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 22:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Koma ine ndine nyongolotsi osati munthu,

      Anthu amandinyogodola* komanso kundinyoza.+

  • Salimo 42:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Anthu amene amadana nane kwambiri akundinyoza,*

      Amandinyoza tsiku lonse kuti: “Mulungu wako ali kuti?”+

  • Salimo 102:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Tsiku lonse adani anga amandinyoza.+

      Anthu amene amanditonza amagwiritsa ntchito dzina langa potemberera ena.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena