Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 32:9, 10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Pakuti anthu a Yehova ndi gawo lake.+

      Yakobo ndiye cholowa chake.+

      10 Anamupeza mʼdziko lachipululu,+

      Mʼchipululu chopanda kanthu, molira zilombo.+

      Anamuzungulira kuti amuteteze, anamusamalira,+

      Ndipo anamuteteza ngati mwana wa diso lake.+

  • Zekariya 2:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Atapatsidwa ulemerero, Mulungu wandituma kwa anthu a mitundu ina amene ankakulandani zinthu zanu,+ chifukwa Yehova wa magulu ankhondo akumwamba wanena kuti, ‘Amene akukukhudzani, akukhudza mwana wa diso langa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena