Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Rute 2:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Yehova akupatse mphoto chifukwa cha zimene wachita,+ ndipo Yehova, Mulungu wa Isiraeli akulipire mokwanira* popeza wathawira mʼmapiko mwake kuti upeze chitetezo.”+

  • Salimo 36:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Inu Mulungu, chikondi chanu chokhulupirika ndi chamtengo wapatali!+

      Ana a anthu amabisala mumthunzi wa mapiko anu.+

  • Salimo 57:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 57 Ndikomereni mtima inu Mulungu, ndikomereni mtima,

      Chifukwa ine ndathawira kwa inu.+

      Ndathawira mumthunzi wa mapiko anu mpaka mavuto atadutsa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena