Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Rute 2:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Yehova akupatse mphoto chifukwa cha zimene wachita,+ ndipo Yehova, Mulungu wa Isiraeli akulipire mokwanira* popeza wathawira mʼmapiko mwake kuti upeze chitetezo.”+

  • Salimo 17:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Nditetezeni ngati mwana wa diso lanu,+

      Ndibiseni mumthunzi wa mapiko anu.+

  • Salimo 91:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Adzakuphimba ndi mapiko ake,

      Ndipo udzathawira pansi pa mapiko ake.*+

      Kukhulupirika kwake+ kudzakhala chishango chako chachikulu+ komanso khoma lokuteteza.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena