-
2 Samueli 20:1Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
20 Ndiyeno panali munthu wina wosokoneza dzina lake Sheba,+ mwana wamwamuna wa Bikiri,+ wafuko la Benjamini. Iye analiza lipenga la nyanga ya nkhosa nʼkunena kuti: “Ife Davide tilibe naye ntchito ndipo sitingapatsidwe cholowa kuchokera kwa mwana wa Jese.+ Aisiraeli inu, aliyense apite kwa milungu* yake!”+
-