Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 20:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Ndiyeno panali munthu wina wosokoneza dzina lake Sheba,+ mwana wamwamuna wa Bikiri,+ wafuko la Benjamini. Iye analiza lipenga la nyanga ya nkhosa nʼkunena kuti: “Ife Davide tilibe naye ntchito ndipo sitingapatsidwe cholowa kuchokera kwa mwana wa Jese.+ Aisiraeli inu, aliyense apite kwa milungu* yake!”+

  • 2 Samueli 22:5, 6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Mafunde a imfa anandizungulira;+

      Gulu la anthu opanda pake linkandiopseza.+

       6 Zingwe za Manda* zinandizungulira;+

      Ndinatcheredwa misampha ya imfa.+

  • Salimo 22:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Adani anga andizungulira ngati agalu.+

      Andizungulira ngati gulu la anthu ochita zoipa,+

      Mofanana ndi mkango, iwo akundiluma manja ndi mapazi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena