Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 27:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Atamukhomerera pamtengo, anagawana malaya ake akunja pochita maere+

  • Yohane 20:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Choncho ophunzira enawo anamuuza kuti: “Ife tawaona Ambuye!” Koma iye anawayankha kuti: “Ndikapanda kuona mabala a misomali mʼmanja mwawo ndi kuika chala changa mʼmabala a misomaliwo ndiponso kuika dzanja langa munthiti mwawo,+ ndithu ine sindikhulupirira.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena