Numeri 15:39 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 39 ‘Zovala zanu zizikhala ndi ulusi kuti mukaziona muzikumbukira malamulo onse a Yehova ndi kuwasunga.+ Musamatsatire zilakolako za mitima yanu ndi maso anu, chifukwa nʼzimene zikukupangitsani kuti musakhale okhulupirika kwa ine.*+ Miyambo 4:25 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 25 Maso ako aziyangʼana patsogolo.Inde, uziyangʼanitsitsa* zinthu zimene zili patsogolo pako.+ Miyambo 23:4, 5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Usadzitopetse pofuna kupeza chuma.+ Leka kuchita zimenezi, mʼmalomwake uzisonyeza kuti ndiwe womvetsa zinthu.* 5 Ukayangʼana pamene panali chumacho, umapeza kuti palibe,+Chifukwa ndithu chimamera mapiko ngati chiwombankhanga nʼkuulukira mʼmwamba.+
39 ‘Zovala zanu zizikhala ndi ulusi kuti mukaziona muzikumbukira malamulo onse a Yehova ndi kuwasunga.+ Musamatsatire zilakolako za mitima yanu ndi maso anu, chifukwa nʼzimene zikukupangitsani kuti musakhale okhulupirika kwa ine.*+
4 Usadzitopetse pofuna kupeza chuma.+ Leka kuchita zimenezi, mʼmalomwake uzisonyeza kuti ndiwe womvetsa zinthu.* 5 Ukayangʼana pamene panali chumacho, umapeza kuti palibe,+Chifukwa ndithu chimamera mapiko ngati chiwombankhanga nʼkuulukira mʼmwamba.+