1 Mafumu 3:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Mundipatse ine mtumiki wanu mtima womvera kuti ndiweruze anthu anu+ komanso ndizitha kusiyanitsa zabwino ndi zoipa.+ Ndani angathe kuweruza anthu anu ambirimbiriwa?”* Salimo 94:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Kodi amene amalangiza mitundu ya anthu, sangathe kudzudzula?+ Iye ndi amene amaphunzitsa anthu kuti akhale ozindikira.+ Danieli 2:21 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 21 Iye amasintha nthawi ndi nyengo,+Amachotsa mafumu komanso kuika mafumu,+Amapereka nzeru kwa anthu anzeru ndiponso amachititsa kuti anthu ozindikira adziwe zinthu.+ Afilipi 1:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Ndipo ine ndikupitiriza kupemphera kuti chikondi chanu chipitirize kukula kwambiri,+ limodzi ndi kudziwa zinthu molondola+ komanso kuzindikira zinthu bwino kwambiri.+
9 Mundipatse ine mtumiki wanu mtima womvera kuti ndiweruze anthu anu+ komanso ndizitha kusiyanitsa zabwino ndi zoipa.+ Ndani angathe kuweruza anthu anu ambirimbiriwa?”*
10 Kodi amene amalangiza mitundu ya anthu, sangathe kudzudzula?+ Iye ndi amene amaphunzitsa anthu kuti akhale ozindikira.+
21 Iye amasintha nthawi ndi nyengo,+Amachotsa mafumu komanso kuika mafumu,+Amapereka nzeru kwa anthu anzeru ndiponso amachititsa kuti anthu ozindikira adziwe zinthu.+
9 Ndipo ine ndikupitiriza kupemphera kuti chikondi chanu chipitirize kukula kwambiri,+ limodzi ndi kudziwa zinthu molondola+ komanso kuzindikira zinthu bwino kwambiri.+