Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 25:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Yehova ndi wabwino komanso wolungama.+

      Nʼchifukwa chake amalangiza ochimwa kuti ayende mʼnjira yoyenera.+

  • Yesaya 28:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Mulungu amaphunzitsa* munthu mʼnjira yoyenerera

      Mulungu wake amamulangiza.+

  • Yohane 6:45
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 45 Zinalembedwa mʼMabuku a Aneneri kuti: ‘Onse adzaphunzitsidwa ndi Yehova.’*+ Aliyense amene wamva kwa Atate ndipo waphunzira amabwera kwa ine.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena