Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 19:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Chilamulo cha Yehova ndi changwiro,+ chimabwezeretsa mphamvu.*+

      Zikumbutso za Yehova ndi zodalirika,+ zimapatsa nzeru munthu wosadziwa zinthu.+

  • Salimo 19:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Nʼzosilirika kuposa golide,

      Kuposa golide wambiri woyengeka bwino.+

      Ndipo nʼzotsekemera kuposa uchi,+ kuposa uchi umene ukukha mʼzisa.

  • Miyambo 3:13-15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Wosangalala ndi munthu amene amapeza nzeru,+

      Ndiponso munthu amene amaphunzira zinthu zimene zingamuthandize kukhala wozindikira.

      14 Chifukwa kupeza nzeru nʼkwabwino kuposa kupeza siliva,

      Ndipo kukhala nazo monga phindu nʼkwabwino kuposa kukhala ndi golide.+

      15 Nʼzamtengo wapatali kuposa miyala ya korali,*

      Palibe chimene umalakalaka chimene chingafanane nazo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena