Salimo 19:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Chilamulo cha Yehova ndi changwiro,+ chimabwezeretsa mphamvu.*+ Zikumbutso za Yehova ndi zodalirika,+ zimapatsa nzeru munthu wosadziwa zinthu.+ Salimo 19:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Nʼzosilirika kuposa golide,Kuposa golide wambiri woyengeka bwino.+Ndipo nʼzotsekemera kuposa uchi,+ kuposa uchi umene ukukha mʼzisa. Miyambo 24:13, 14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Mwana wanga, idya uchi chifukwa ndi wabwino.Uchi wochokera pazisa za njuchi umatsekemera. 14 Mofanana ndi zimenezi, dziwa kuti nzeru ndi zabwino kwa iwe.*+ Ukazipeza, udzakhala ndi tsogolo labwinoNdipo chiyembekezo chako sichidzawonongedwa.+
7 Chilamulo cha Yehova ndi changwiro,+ chimabwezeretsa mphamvu.*+ Zikumbutso za Yehova ndi zodalirika,+ zimapatsa nzeru munthu wosadziwa zinthu.+
10 Nʼzosilirika kuposa golide,Kuposa golide wambiri woyengeka bwino.+Ndipo nʼzotsekemera kuposa uchi,+ kuposa uchi umene ukukha mʼzisa.
13 Mwana wanga, idya uchi chifukwa ndi wabwino.Uchi wochokera pazisa za njuchi umatsekemera. 14 Mofanana ndi zimenezi, dziwa kuti nzeru ndi zabwino kwa iwe.*+ Ukazipeza, udzakhala ndi tsogolo labwinoNdipo chiyembekezo chako sichidzawonongedwa.+