Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 97:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Kuwala kwaunikira olungama+

      Ndipo owongoka mtima akusangalala.

  • Yesaya 42:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Anthu amene ali ndi vuto losaona ndidzawatsogolera kuti ayende mʼnjira imene sakuidziwa.+

      Ndidzawadutsitsa mʼnjira zachilendo.+

      Mdima ndidzausandutsa kuwala pamaso pawo+

      Ndipo malo okumbikakumbika ndidzawasalaza.+

      Zimenezi ndi zimene ndidzawachitire ndipo sindidzawasiya.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena