-
Yesaya 63:7Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
7 Ndidzanena za ntchito za Yehova zosonyeza chikondi chake chokhulupirika,
Ntchito zotamandika za Yehova,
Chifukwa cha zinthu zonse zimene Yehova watichitira.+
Zinthu zabwino zambiri zimene wachitira nyumba ya Isiraeli,
Mogwirizana ndi chifundo chake komanso chikondi chake chokhulupirika chomwe ndi chochuluka.
-