Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 7:15-17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Ndipo chikondi changa chokhulupirika sichidzachoka pa iye ngati mmene ndinachichotsera pa Sauli,+ amene ndinamʼchotsa pamaso pako. 16 Nyumba yako ndi ufumu wako zidzakhalapobe mpaka kalekale. Mpando wako wachifumu udzakhazikika mpaka kalekale.”’”+

      17 Natani anauza Davide mawu onsewa ndiponso masomphenya onse amene anaona.+

  • 1 Mafumu 3:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Solomo atamva zimenezi anati: “Inu mwasonyeza kwambiri chikondi chokhulupirika kwa mtumiki wanu Davide bambo anga, chifukwa anali wokhulupirika, wachilungamo komanso wowongoka mtima pamaso panu. Mwapitiriza kumusonyeza chikondi chimenechi mpaka pano pomupatsa mwana kuti akhale pampando wake wachifumu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena