Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 9:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Ndiyeno Mose anatambasula dzanja lake nʼkuloza kumwamba ndi ndodo yake. Atatero, Yehova anachititsa mabingu ndipo anagwetsa matalala ndi moto* padziko lapansi. Choncho Yehova anapitiriza kugwetsa matalala mʼdziko la Iguputo.

  • Salimo 107:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Aona mmene mawu ake amayambitsira mphepo yamkuntho,+

      Nʼkuchititsa mafunde panyanja.

  • Yesaya 30:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Yehova adzapangitsa kuti mawu ake aulemerero+ amveke

      Ndipo adzapangitsa kuti dzanja lake+ limene likutsika ndi mkwiyo waukulu lionekere.+

      Dzanjalo lidzatsika ndi moto wowononga,+

      Mvula yamphamvu,+ mphezi komanso mvula yamatalala.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena