Ekisodo 15:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Yehova ndi msilikali wamphamvu.+ Dzina lake ndi Yehova.+ 1 Samueli 17:47 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 47 Ndipo onse amene asonkhana panowa adziwa* kuti Yehova sapulumutsa ndi lupanga kapena mkondo,+ chifukwa Yehova ndiye mwini nkhondo,+ ndipo nonsenu akuperekani mʼmanja mwathu.”+ 2 Mbiri 20:15 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 15 Choncho Yahazieli anati: “Tamverani Ayuda nonsenu, anthu a ku Yerusalemu ndi inu Mfumu Yehosafati! Yehova akukuuzani kuti, ‘Musaope kapena kuchita mantha ndi gulu lalikululi chifukwa nkhondoyi si yanu, ndi ya Mulungu.+ Yesaya 42:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Yehova adzapita kunkhondo ngati munthu wamphamvu.+ Iye adzachita zinthu modzipereka kwambiri ngati msilikali.+ Adzafuula, inde adzafuula ngati anthu amene akupita kunkhondo.Iye adzasonyeza kuti ndi wamphamvu kwambiri kuposa adani ake.+
47 Ndipo onse amene asonkhana panowa adziwa* kuti Yehova sapulumutsa ndi lupanga kapena mkondo,+ chifukwa Yehova ndiye mwini nkhondo,+ ndipo nonsenu akuperekani mʼmanja mwathu.”+
15 Choncho Yahazieli anati: “Tamverani Ayuda nonsenu, anthu a ku Yerusalemu ndi inu Mfumu Yehosafati! Yehova akukuuzani kuti, ‘Musaope kapena kuchita mantha ndi gulu lalikululi chifukwa nkhondoyi si yanu, ndi ya Mulungu.+
13 Yehova adzapita kunkhondo ngati munthu wamphamvu.+ Iye adzachita zinthu modzipereka kwambiri ngati msilikali.+ Adzafuula, inde adzafuula ngati anthu amene akupita kunkhondo.Iye adzasonyeza kuti ndi wamphamvu kwambiri kuposa adani ake.+