Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 51:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Nsembe zimene Mulungu amasangalala nazo ndi kudzimvera chisoni mumtima.

      Inu Mulungu, simudzakana* mtima wosweka ndi wophwanyika.+

  • Yesaya 57:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Chifukwa Wapamwamba ndi Wokwezeka,

      Amene adzakhalepo mpaka kalekale+ ndiponso dzina lake ndi loyera,+ wanena kuti:

      “Ine ndimakhala pamalo apamwamba komanso oyera,+

      Koma ndimakhalanso ndi anthu opsinjika ndiponso amene ali ndi mtima wodzichepetsa,

      Kuti nditsitsimutse mtima wa anthu onyozeka

      Ndiponso kuti nditsitsimutse mtima wa anthu opsinjika.+

  • Yesaya 66:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 “Dzanja langa ndi limene linapanga zinthu zonsezi,

      Ndipo izi ndi zimene zinachitika kuti zonsezi zikhalepo,” akutero Yehova.+

      “Choncho ine ndidzayangʼana munthu ameneyu,

      Ndidzayangʼana munthu wodzichepetsa ndiponso wosweka mtima amene amadera nkhawa mawu anga.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena