Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 37:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Yehova amadziwa mavuto amene anthu osalakwa akukumana nawo,*

      Ndipo cholowa chawo chidzakhalapo mpaka kalekale.+

  • Yeremiya 12:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Koma inu Yehova, mukundidziwa bwino+ ndipo mumandiona.

      Mwafufuza mtima wanga ndipo mwapeza kuti ndine wokhulupirika kwa inu.+

      Apatuleni ngati nkhosa zimene zikukaphedwa,

      Ndipo muwaike padera poyembekezera tsiku limene adzaphedwe.

  • 1 Petulo 3:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Maso a Yehova* ali pa olungama, ndipo makutu ake amamva mapemphero awo opembedzera,+ koma Yehova* amakwiyira anthu amene amachita zoipa.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena