Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 25:39
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 39 Davide atamva kuti Nabala wamwalira ananena kuti: “Adalitsike Yehova amene wandiweruzira mlandu+ wa mawu onyoza a Nabala,+ komanso wandiletsa ine mtumiki wake kuti ndisachite choipa chilichonse.+ Yehova wabwezera zoipa za Nabala pamutu pake!” Kenako Davide anatuma anthu kuti akamufunsirire Abigayeli kuti akhale mkazi wake.

  • Salimo 52:4, 5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Umakonda mawu onse opweteka ena,

      Iwe amene lilime lako limalankhula zachinyengo.

       5 Nʼchifukwa chake Mulungu adzakugwetsa ndipo sudzakhalakonso.+

      Adzakugwira nʼkukukokera kutali ndi tenti yako,+

      Ndipo adzakuzula nʼkukuchotsa mʼdziko la anthu amoyo.+ (Selah)

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena