Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 22:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Makolo athu ankadalira inu.+

      Iwo ankakudalirani ndipo inu munkawapulumutsa.+

  • Danieli 3:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Ngati mungatiponyere mungʼanjo yoyaka moto, Mulungu wathu amene tikumutumikira akhoza kutipulumutsa. Iye akhozanso kutipulumutsa mʼmanja mwanu mfumu.+

  • Danieli 6:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Mfumu inasangalala kwambiri ndipo inalamula kuti Danieli amutulutse mʼdzenjemo. Danieli anatulutsidwadi mʼdzenjemo ndipo sanavulale paliponse chifukwa anakhulupirira Mulungu wake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena