Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 37:40
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 40 Yehova adzawathandiza nʼkuwapulumutsa.+

      Adzawalanditsa kwa oipa nʼkuwapulumutsa,

      Chifukwa athawira kwa iye.+

  • Miyambo 18:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Dzina la Yehova ndi nsanja yolimba.+

      Wolungama amathawira mmenemo ndipo amatetezedwa.*+

  • Danieli 3:26, 27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Nebukadinezara anayandikira khomo la ngʼanjo yoyaka motoyo nʼkunena kuti: “Shadireki, Misheki ndi Abedinego, inu atumiki a Mulungu Wamʼmwambamwamba,+ tulukani ndipo mubwere kuno!” Atatero, Shadireki, Misheki ndi Abedinego anatuluka pakati pa motowo. 27 Masatarapi, akuluakulu a boma, abwanamkubwa ndi nduna zapamwamba za mfumu amene anasonkhana kumeneko,+ anaona kuti amuna amenewa+ motowo sunawawotche* ngakhale pangʼono. Tsitsi la kumutu kwawo ndi limodzi lomwe silinawauke. Zovala zawo sizinasinthe ndipo sankamveka ngakhale fungo la moto.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena