Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 54:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Taonani! Mulungu ndi amene amandithandiza.+

      Yehova amadalitsa anthu amene akundithandiza.

  • Yesaya 50:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Koma Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, adzandithandiza.+

      Nʼchifukwa chake sindidzamva kuti ndanyozeka.

      Nʼchifukwa chake ndalimbitsa nkhope yanga ngati mwala wa nsangalabwi,+

      Ndipo ndikudziwa kuti sindidzachititsidwa manyazi.

  • Aheberi 13:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Tikhale olimba mtima ndithu ndipo tinene kuti: “Yehova* ndi amene amandithandiza. Sindidzaopa. Munthu angandichite chiyani?”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena