Ekisodo 15:17 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 17 Mudzawabweretsa nʼkuwakhazikitsa mʼphiri limene ndi cholowa chanu.+Malo okhazikika amene mwakonzeratu kuti mukhalemo, inu Yehova.Malo opatulika amene manja anu, inu Yehova, anakhazikitsa. Salimo 78:55 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 55 Iye anathamangitsa mitundu ya anthu kuichotsa pamaso pawo.+Iye anawagawira dzikolo kuti likhale cholowa chawo pochita kuwayezera ndi chingwe.+Anachititsa mafuko a Isiraeli kuti akhale mʼnyumba zawozawo.+ Salimo 80:8, 9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 8 Munachititsa kuti mtengo wa mpesa+ uchoke mu Iguputo. Munathamangitsa mitundu ya anthu kuti mudzalemo mtengowo.+ 9 Munalambula malo odzalapo mtengo wa mpesawo,Ndipo unazika mizu nʼkudzaza dziko.+
17 Mudzawabweretsa nʼkuwakhazikitsa mʼphiri limene ndi cholowa chanu.+Malo okhazikika amene mwakonzeratu kuti mukhalemo, inu Yehova.Malo opatulika amene manja anu, inu Yehova, anakhazikitsa.
55 Iye anathamangitsa mitundu ya anthu kuichotsa pamaso pawo.+Iye anawagawira dzikolo kuti likhale cholowa chawo pochita kuwayezera ndi chingwe.+Anachititsa mafuko a Isiraeli kuti akhale mʼnyumba zawozawo.+
8 Munachititsa kuti mtengo wa mpesa+ uchoke mu Iguputo. Munathamangitsa mitundu ya anthu kuti mudzalemo mtengowo.+ 9 Munalambula malo odzalapo mtengo wa mpesawo,Ndipo unazika mizu nʼkudzaza dziko.+