Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 23:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Inu musanafike, ndidzachititsa anthuwo mantha*+ ndipo Ahivi, Akanani ndi Ahiti adzathawiratu pamaso panu.+

  • Ekisodo 23:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Ndidzawathamangitsa pamaso panu pangʼonopangʼono mpaka mutaberekana ndi kulanda dzikolo.+

  • Yoswa 24:12, 13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Ndinawachititsa mantha inu musanafike, choncho anakuthawani+ ngati mmene anachitira mafumu awiri a Aamori. Iwo sanathawe chifukwa cha lupanga lanu kapena chifukwa cha uta wanu.+ 13 Ndinakupatsani dziko limene simunalikhetsere thukuta komanso mizinda imene simunaimange,+ ndipo munayamba kukhalamo. Mukudyanso zipatso za mitengo ya mpesa ndi mitengo ya maolivi imene simunadzale.’+

  • 1 Mafumu 4:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Ayuda ndi Aisiraeli ankakhala mwamtendere. Aliyense ankakhala pansi pa mtengo wake wa mpesa ndi mtengo wake wa mkuyu, kuchokera ku Dani mpaka ku Beere-seba, masiku onse a Solomo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena