Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 93:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Ulemerero wa Yehova ndi waukulu kumwamba,

      Kuposa mkokomo wa madzi ambiri,+

      Ndi wamphamvu kuposa mafunde amphamvu amʼnyanja.+

  • Yeremiya 5:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 ‘Kodi simukuchita nane mantha?’ akutero Yehova.

      ‘Kodi simukunjenjemera pamaso panga?

      Ine ndi amene ndinaika mchenga kuti ukhale malire a nyanja,

      Malire amene adzakhalepo mpaka kalekale.

      Ngakhale kuti mafunde ake amawinduka, sangadutse malirewo.

      Ndipo ngakhale amachita phokoso, sangapitirire malirewo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena