Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 32:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Pamapeto pake ndinaulula tchimo langa kwa inu,

      Sindinabise cholakwa changa.+

      Ndinati: “Ndidzaulula machimo anga kwa Yehova.”+

      Ndipo inu munandikhululukira zolakwa zanga ndi machimo anga.+ (Selah)

  • Salimo 40:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Masoka amene andizungulira ndi ambiri moti sindingathe kuwawerenga.+

      Zolakwa zanga ndi zochuluka moti sindikutha kuona kumene ndikulowera.+

      Zachuluka kwambiri kuposa tsitsi lakumutu kwanga,

      Ndipo ndataya mtima.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena