Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 25:32, 33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Zitatero, Davide anauza Abigayeli kuti: “Atamandike Yehova Mulungu wa Isiraeli, amene wakutumiza kudzakumana ndi ine lero! 33 Iwenso udalitsike chifukwa cha kuganiza bwino kwako. Udalitsike chifukwa chondiletsa kuti ndisapalamule mlandu wa magazi+ ndiponso kuti ndisabwezere* ndekha ndi manja anga.

  • Miyambo 24:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Ukamatsatira malangizo anzeru udzatha kumenya nkhondo yako,+

      Ndipo pakakhala alangizi* ambiri udzapambana.*+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena