Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 2:23, 24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Kenako Mfumu Solomo analumbira pamaso pa Yehova kuti: “Mulungu andilange mowirikiza ngati Adoniya sanaike moyo wake pangozi popempha zimenezi. 24 Ndikulumbira mʼdzina la Yehova Mulungu wamoyo, amene anandiika pampando wachifumu wa Davide bambo anga komanso amene anachititsa kuti ufumu wanga ukhazikike+ ndiponso kuti pakhale mzere wa banja lachifumu+ mogwirizana ndi zimene analonjeza, lero Adoniya aphedwa.”+

  • Salimo 5:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Mudzawononga anthu amene amalankhula mabodza.+

      Yehova amadana ndi anthu achiwawa komanso achinyengo.*+

  • Mlaliki 5:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Usalole kuti pakamwa pako pakuchimwitse,+ komanso usamauze mngelo* kuti unalakwitsa.+ Nʼchifukwa chiyani ukufuna kukwiyitsa Mulungu woona ndi zonena zako mpaka kufika poti awononge ntchito ya manja ako?+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena