Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Nehemiya 6:2, 3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 nthawi yomweyo Sanibalati ndi Gesemu ananditumizira uthenga wakuti: “Bwera tidzapangane nthawi yoti tikakumane mʼmudzi wina mʼchigwa cha Ono.”+ Koma ankandikonzera chiwembu. 3 Choncho ndinatumiza anthu kuti akawauze kuti: “Ntchito imene ndikugwirayi ndi yaikulu ndipo sindingathe kubwera. Kodi ntchitoyi iime chifukwa chakuti ine ndabwera kumeneko?”

  • Miyambo 27:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Munthu wochenjera akaona tsoka amabisala,+

      Koma wosadziwa zinthu amangopitabe ndipo amakumana ndi mavuto.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena