Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 37:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Zinthu zochepa zimene munthu wolungama ali nazo ndi zabwino

      Kusiyana ndi zinthu zochuluka za anthu ambiri oipa.+

  • Yeremiya 17:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Munthu amene amapeza chuma mwachinyengo,*+

      Ali ngati nkhwali imene imasonkhanitsa mazira amene sinaikire.

      Chuma chakecho chidzatha asanakwanitse hafu ya zaka za moyo wake,

      Ndipo pamapeto pake adzadziwika kuti ndi wopusa.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena