Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Miyambo 17:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Ndi bwino kudya mkate wouma pali mtendere,*+

      Kusiyana ndi kuchita maphwando ochuluka* mʼnyumba imene muli mikangano.+

  • Miyambo 21:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Ndi bwino kukhala mʼchipululu

      Kusiyana ndi kukhala ndi mkazi wolongolola* komanso wosachedwa kukwiya.+

  • Miyambo 25:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Ndi bwino kukhala pakona ya denga la nyumba

      Kusiyana ndi kukhala mʼnyumba limodzi ndi mkazi wolongolola.*+

  • Miyambo 27:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Mkazi wolongolola* ali ngati denga limene limadontha nthawi zonse pa tsiku la mvula.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena