Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Miyambo 10:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Miyambi ya Solomo.+

      Mwana wanzeru amasangalatsa bambo ake,+

      Koma mwana wopusa amamvetsa chisoni mayi ake.

  • Miyambo 23:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Mwana wanga, mtima wako ukakhala wanzeru,

      Ndithu mtima wanga udzasangalala.+

  • 2 Yohane 4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Ndikusangalala kwambiri chifukwa ndapeza ena mwa ana anu akuyenda mʼchoonadi+ mogwirizana ndi lamulo limene tinalandira kwa Atate.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena