Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 9:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Iye akalanda chinthu, ndani angalimbane naye?

      Ndani angamufunse kuti, ‘Mukuchita chiyani?’+

  • Yesaya 14:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Yehova wa magulu ankhondo akumwamba wasankha zoti achite,

      Ndiye ndi ndani amene angazilepheretse?+

      Dzanja lake latambasulidwa,

      Ndi ndani amene angalibweze?+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena