Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mbiri 6:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Anthu anu akakuchimwirani (popeza palibe munthu amene sachimwa)+ inu nʼkuwakwiyira kwambiri ndiponso kuwapereka kwa adani, adani awowo nʼkuwatenga kupita nawo kudziko lakutali kapena lapafupi,+

  • Salimo 51:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Taonani! Ndinabadwa ndili wochimwa,

      Ndipo ndine wochimwa kuchokera pamene mayi anga anatenga pakati panga.+

  • Aroma 3:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Popeza anthu onse ndi ochimwa ndipo amalephera kusonyeza bwinobwino ulemerero wa Mulungu.+

  • 1 Yohane 1:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Tikamanena kuti, “Tilibe uchimo,” ndiye kuti tikudzinamiza+ ndipo mumtima mwathu mulibe choonadi.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena