Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 1:13, 14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Choncho Aiguputo anakakamiza Aisiraeli kuti azigwira ntchito yaukapolo mwankhanza.+ 14 Iwo anasautsa moyo wa Aisiraeliwo powagwiritsa ntchito yowawa, yomwe inali yoponda matope ndi kuumba njerwa. Anawagwiritsa ntchito yaukapolo wa mtundu uliwonse mʼmunda. Ankawazunza komanso kuwagwiritsa ntchito ya mtundu uliwonse wa ukapolo.+

  • Mika 7:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Manja awo amachita zoipa ndipo amazichita mwaukatswiri kwambiri.+

      Kalonga amalamula kuti amupatse mphatso,

      Woweruza amauza anthu kuti amupatse chiphuphu.+

      Munthu wotchuka amauza anthu zimene akulakalaka,+

      Ndipo onsewa amakonzera limodzi chiwembu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena