Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 28:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Koma kodi nzeru zingapezeke kuti?+

      Ndipo kumvetsa zinthu kumachokera kuti?+

  • Mlaliki 7:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Zimene zinachitika kale sitingathe kuzimvetsa ndipo nʼzozama kwambiri. Ndi ndani angazimvetse?+

  • Mlaliki 11:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Iwe sudziwa mmene mzimu umachititsira kuti mafupa a mwana amene ali mʼmimba mwa mayi ake akule.+ Mofanana ndi zimenezi sudziwanso ntchito ya Mulungu woona, amene amachita zinthu zonse.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena