Deuteronomo 12:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Inuyo ndi mabanja anu muzidzadya zimenezi kumalo amenewo pamaso pa Yehova Mulungu wanu,+ ndipo muzidzasangalala ndi zochita zanu zonse+ chifukwa Yehova Mulungu wanu wakudalitsani. Salimo 104:15 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 15 Komanso kuti mutuluke vinyo amene amasangalatsa mtima wa munthu,+Mafuta amene amachititsa kuti nkhope ya munthu isalale,Ndiponso chakudya chimene chimapereka mphamvu kwa munthu.*+ Mlaliki 2:24 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 24 Palibe chabwino kwa munthu kuposa kuti adye, amwe ndi kusangalala chifukwa choti wagwira ntchito mwakhama.+ Ndinazindikira kuti zimenezinso nʼzochokera mʼdzanja la Mulungu woona,+
7 Inuyo ndi mabanja anu muzidzadya zimenezi kumalo amenewo pamaso pa Yehova Mulungu wanu,+ ndipo muzidzasangalala ndi zochita zanu zonse+ chifukwa Yehova Mulungu wanu wakudalitsani.
15 Komanso kuti mutuluke vinyo amene amasangalatsa mtima wa munthu,+Mafuta amene amachititsa kuti nkhope ya munthu isalale,Ndiponso chakudya chimene chimapereka mphamvu kwa munthu.*+
24 Palibe chabwino kwa munthu kuposa kuti adye, amwe ndi kusangalala chifukwa choti wagwira ntchito mwakhama.+ Ndinazindikira kuti zimenezinso nʼzochokera mʼdzanja la Mulungu woona,+