-
Deuteronomo 12:18Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
18 Koma muzidzadya zinthu zimenezi pamaso pa Yehova Mulungu wanu, pamalo amene Yehova Mulungu wanu adzasankhe.+ Muzidzadya zinthuzi inuyo, mwana wanu wamwamuna, mwana wanu wamkazi, kapolo wanu wamwamuna, kapolo wanu wamkazi ndi Mlevi amene akukhala mumzinda wanu.* Ndipo muzidzasangalala pamaso pa Yehova Mulungu wanu ndi zochita zanu zonse.
-