-
Mlaliki 9:11Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
11 Ndaonanso chinthu china padziko lapansi pano kuti si nthawi zonse pamene anthu othamanga kwambiri amapambana pampikisano komanso pamene amphamvu amapambana pankhondo.+ Si nthawi zonse pamene anthu ochenjera amapeza chakudya, ndiponso si nthawi zonse pamene anthu anzeru amakhala ndi chuma.+ Komanso anthu odziwa zinthu, si nthawi zonse pamene zinthu zimawayendera bwino,+ chifukwa nthawi yatsoka komanso zinthu zosayembekezereka zimagwera onsewo.
-