Miyambo 14:8 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 8 Nzeru zimathandiza munthu wochenjera kuzindikira njira imene akuyenda,Koma anthu opusa amapusitsika* ndi kupusa kwawo komwe.+ Miyambo 17:24 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 24 Munthu wozindikira amakhala ndi cholinga choti apeze nzeru,Koma maso a munthu wopusa amangoyendayenda mpaka kumalekezero a dziko lapansi.+ Yohane 3:19 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 19 Kuwala kwafika mʼdziko+ koma mʼmalo mokonda kuwala anthu akukonda mdima popeza ntchito zawo nʼzoipa, nʼchifukwa chake adzaweruzidwe. 1 Yohane 2:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Koma amene amadana ndi mʼbale wake ali mumdima ndipo akuyenda mumdimawo+ komanso sakudziwa kumene akupita+ popeza maso ake sakuona chifukwa cha mdimawo.
8 Nzeru zimathandiza munthu wochenjera kuzindikira njira imene akuyenda,Koma anthu opusa amapusitsika* ndi kupusa kwawo komwe.+
24 Munthu wozindikira amakhala ndi cholinga choti apeze nzeru,Koma maso a munthu wopusa amangoyendayenda mpaka kumalekezero a dziko lapansi.+
19 Kuwala kwafika mʼdziko+ koma mʼmalo mokonda kuwala anthu akukonda mdima popeza ntchito zawo nʼzoipa, nʼchifukwa chake adzaweruzidwe.
11 Koma amene amadana ndi mʼbale wake ali mumdima ndipo akuyenda mumdimawo+ komanso sakudziwa kumene akupita+ popeza maso ake sakuona chifukwa cha mdimawo.