Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 30:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Anthu akadzayamba kukhala ku Ziyoni, ku Yerusalemu,+ inu simudzaliranso.+ Mulungu adzakukomerani mtima akadzamva kulira kwanu kopempha thandizo. Akadzangomva kulira kwanu, nthawi yomweyo adzakuyankhani.+

  • Yesaya 55:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 55 Inu nonse amene mukumva ludzu,+ bwerani mudzamwe madzi.+

      Inu amene mulibe ndalama, bwerani mudzagule kuti mudye.

      Inde bwerani mudzagule vinyo ndi mkaka+ popanda ndalama ndiponso popanda mtengo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena