Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 30:22, 23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Potsirizira pake, Mulungu anakumbukira Rakele ndipo anamva pemphero lake nʼkumuthandiza kuti ayambe kubereka.*+ 23 Rakele anakhala woyembekezera nʼkubereka mwana wamwamuna. Ndiyeno iye anati: “Mulungu wachotsa kunyozeka kwanga.”+

  • Luka 1:24, 25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Patapita masiku angapo, mkazi wake Elizabeti anakhala woyembekezera ndipo anakhala kwayekha miyezi 5. Iye ananena kuti: 25 “Izitu nʼzimene Yehova* wandichitira masiku ano. Iye wandikumbukira kuti achotse kunyozeka kwanga pamaso pa anthu.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena