Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 7:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Koma Yehova anakutulutsani ndi dzanja lamphamvu kuti akulanditseni mʼnyumba yaukapolo,+ mʼmanja mwa Farao* mfumu ya Iguputo, chifukwa chakuti Yehova anakukondani, komanso chifukwa chosunga lumbiro lake limene analumbirira makolo anu.+

  • Yeremiya 31:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Yehova anaonekera kwa ine ali kutali ndipo anati:

      “Ine ndakukonda ndipo ndidzakukonda mpaka kalekale.

      Nʼchifukwa chake ndakukokera kwa ine ndi chikondi chokhulupirika.*+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena