-
1 Mafumu 18:26Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
26 Choncho anatenga ngʼombe yaingʼono imene anapatsidwa nʼkuikonza ndipo kenako anayamba kuitana dzina la Baala kuyambira mʼmawa mpaka masana. Ankaitana kuti: “Inu a Baala, tiyankheni!” Koma sipanamveke mawu alionse ndipo palibe anayankha.+ Iwo anapitiriza kudumphadumpha uku akuzungulira guwa lansembe limene anamanga.
-