Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 18:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Choncho anatenga ngʼombe yaingʼono imene anapatsidwa nʼkuikonza ndipo kenako anayamba kuitana dzina la Baala kuyambira mʼmawa mpaka masana. Ankaitana kuti: “Inu a Baala, tiyankheni!” Koma sipanamveke mawu alionse ndipo palibe anayankha.+ Iwo anapitiriza kudumphadumpha uku akuzungulira guwa lansembe limene anamanga.

  • Yesaya 37:37, 38
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 37 Choncho Senakeribu mfumu ya Asuri anachoka nʼkubwerera kukakhala ku Nineve.+ 38 Pamene Senakeribu ankaweramira mulungu wake Nisiroki mʼkachisi, ana ake Adarameleki ndi Sarezere anamupha ndi lupanga+ nʼkuthawira kudziko la Ararati.+ Kenako mwana wake Esari-hadoni+ anakhala mfumu mʼmalo mwake.

  • Yona 1:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Oyendetsa chombo anachita mantha kwambiri ndipo aliyense anayamba kuitana mulungu wake kuti amuthandize. Iwo anayamba kuponya mʼnyanja katundu amene anali mʼchombocho kuti chipepukidwe.+ Apa nʼkuti Yona atatsikira mkatikati mwa chombocho nʼkugona tulo tofa nato.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena